Genesis 24:59 - Buku Lopatulika59 Ndipo anamlola Rebeka mlongo wao ndi mlezi wake, amuke pamodzi ndi mnyamata wake wa Abrahamu, ndi anthu ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201459 Ndipo anamlola Rebeka mlongo wao ndi mlezi wake, amuke pamodzi ndi mnyamata wake wa Abrahamu, ndi anthu ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa59 Choncho adamlola Rebeka pamodzi ndi mlezi wake, kuti apite ndi wantchito wa Abrahamu ndi anthu aja omuperekezaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero59 Kotero anamulola Rebeka pamodzi ndi mlezi wake kuti apite ndi wantchito wa Abrahamu pamodzi ndi anthu amene anali naye. Onani mutuwo |