Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:58 - Buku Lopatulika

58 Ndipo anamuitana Rebeka nati kwa iye, Kodi udzanka pamodzi ndi munthuyo? Ndipo anati, Ndidzanka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

58 Ndipo anamuitana Rebeka nati kwa iye, Kodi udzanka pamodzi ndi munthuyo? Ndipo anati, Ndidzanka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

58 Motero adamuitana Rebeka namufunsa kuti, “Kodi ukufuna kupita naye munthuyu?” Rebekayo adayankha kuti, “Inde, ndipita.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

58 Choncho iwo anamuyitana Rebeka uja namufunsa kuti, “Kodi ukufuna kupita ndi munthuyu panopa?” Iye anayankha kuti, “Ndipita.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:58
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anati iwo, Tidzamuitana namwaliyo, tidzamfunsa pakamwa pake.


Ndipo anamlola Rebeka mlongo wao ndi mlezi wake, amuke pamodzi ndi mnyamata wake wa Abrahamu, ndi anthu ake.


Ndipo Maria anati, Onani, mdzakazi wa Ambuye; kukhale kwa ine monga mwa mau anu. Ndipo mngelo anachoka kwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa