Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:43 - Buku Lopatulika

43 taonani, ine ndiima pa kasupe wa madzi, ndipo pakhale, kuti namwali amene atuluka kudzatunga madzi ndimwe pang'ono m'mtsuko mwako;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 taonani, ine ndiima pa kasupe wa madzi, ndipo pakhale, kuti namwali amene atuluka kudzatunga madzi ndimwe pang'ono m'mtsuko mwako;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Ndili pano pachitsime, pakabwera namwali pano kudzatunga madzi, ine ndidzampempha kuti: Chonde patseko madzi a mumtsuko mwako kuti ndimwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 taonani ndayima pambali pa chitsime ichi; ndipo ndidzati kwa namwali amene atabwere kudzatunga kuti, chonde nditamwako madzi a mu mtsuko wakowu,’

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:43
2 Mawu Ofanana  

ndipo iye akati kwa ine, Imwatu iwe, ndiponso ndidzatungira ngamira zako; yemweyo akhale mkazi amene Yehova wamsankhira mwana wa mbuyanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa