Genesis 24:42 - Buku Lopatulika42 Ndipo ndinafika lero kukasupe, ndipo ndinati, Yehova Mulungu wa mbuyanga Abrahamu, ngati mundiyendetsatu bwino njira yanga m'mene ndinkamo ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Ndipo ndinafika lero kukasupe, ndipo ndinati, Yehova Mulungu wa mbuyanga Abrahamu, ngati mundiyendetsatu bwino njira yanga m'mene ndinkamo ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 “Tsono lero lino nditafika ku chitsime, ndinapemphera kuti, ‘Chauta, Mulungu wa mbuyanga Abrahamu, chonde mundithandize kuti ndikhoze pa ulendo wangawu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 “Tsono lero lino pamene ndafika pa chitsime, ndinapempha kuti, ‘Yehova, Mulungu wa mbuye wanga, Abrahamu, ngati Inu mwandidalitsadi pa ulendowu, Onani mutuwo |