Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo ndinati kwa mbuyanga, Kapena mkazi sadzanditsata ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo ndinati kwa mbuyanga, Kapena mkazi sadzanditsata ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Ndipo ine ndidamuyankha mbuyanga kuti, ‘Nanga zidzatani ngati mkaziyo adzakana kubwera nane kuno?’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 “Ndipo ine ndinati kwa mbuye wanga, ‘Nanga mkaziyo akakapanda kubwera nane pamodzi?’

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:39
2 Mawu Ofanana  

koma udzanke kunyumba ya atate wanga, kwa abale anga, ndi kumtengera mwana wanga mkazi.


Ndipo anati kwa iye mnyamatayo, Kapena sadzafuna mkaziyo kunditsata ine ku dziko lino: kodi ndikambwezerenso mwana wanu ku dziko komwe mwachokera inu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa