Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:38 - Buku Lopatulika

38 koma udzanke kunyumba ya atate wanga, kwa abale anga, ndi kumtengera mwana wanga mkazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 koma udzanke kunyumba ya atate wanga, kwa abale anga, ndi kumtengera mwana wanga mkazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Koma upite kwathu kwa atate anga ndi achibale anga, kukamutengera mkazi mwana wanga kumeneko.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 koma upite ku banja la abambo anga ndi kwa abale anga kuti ukamupezere mkazi mwana wanga.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:38
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa Abramu, Tuluka iwe m'dziko lako, ndi kwa abale ako, ndi kunyumba ya atate wako, kunka ku dziko limene ndidzakusonyeza iwe;


Ndipo mbuyanga anandilumbiritsa ine kuti, Usamtengere mwana wanga mkazi wa ana aakazi a Kanani, m'dziko mwao m'mene ndikhala ine;


Ndipo ndinati kwa mbuyanga, Kapena mkazi sadzanditsata ine.


Koma udzanke ku dziko langa, kwa abale anga, ndi kumtengera mwana wanga Isaki mkazi.


Ndipo Labani ananka kukasenga nkhosa zake: ndipo Rakele anaba aterafi a atate wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa