Genesis 24:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo mbuyanga anandilumbiritsa ine kuti, Usamtengere mwana wanga mkazi wa ana aakazi a Kanani, m'dziko mwao m'mene ndikhala ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo mbuyanga anandilumbiritsa ine kuti, Usamtengere mwana wanga mkazi wa ana akazi a Kanani, m'dziko mwao m'mene ndikhala ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsono mbuyanga adandilumbiritsa kuti ndisunge mau ake akuti, ‘Mwana wangayu usadzamfunire mbeta pakati pa anamwali a dziko lino la Kanani, kumene ndili ine kuno. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Tsono mbuye wanga anandilumbiritsa kuti ndisunge mawu ake akuti, ‘Usadzamupezere mwana wanga mkazi kuchokera mwa atsikana a dziko lino la Kanaani, Onani mutuwo |