Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo Sara mkazi wake wa mbuyanga anambalira mbuyanga mwana wamwamuna, mkaziyo anali wokalamba; ndipo anampatsa mwanayo zonse ali nazo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo Sara mkazi wake wa mbuyanga anambalira mbuyanga mwana wamwamuna, mkaziyo anali wokalamba; ndipo anampatsa mwanayo zonse ali nazo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Sara, mkazi wake wa mbuyanga, adamubalira mwana wamwamuna, Sarayo atakalamba kale. Ndipo mbuyangayo wamupatsa chuma chake chonse mwana ameneyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Sara, mkazi wa mbuye wanga anamubalira iye mwana wamwamuna ngakhale kuti Sarayo anali wokalamba. Tsono mbuye wanga wamupatsa mwanayo chuma chonse.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:36
7 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake anati kwa Abrahamu, Chotsa mdzakazi uyo, ndi mwana wake wamwamuna; chifukwa mwana wa mdzakazi uyo sadzalowa m'nyumba pamodzi naye mwana wanga Isaki.


Ndipo Abrahamu anampatsa Isaki zonse anali nazo.


Ndipo iye osafooka m'chikhulupiriro sanalabadire thupi lake, ndilo longa ngati lakufa pamenepo, (pokhala iye ngati zaka makumi khumi), ndi mimba ya Sara idaumanso;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa