Genesis 24:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Rebeka anali ndi mlongo wake dzina lake Labani; ndipo Labani anathamangira munthuyo kunja ku kasupe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Rebeka anali ndi mlongo wake dzina lake Labani; ndipo Labani anathamangira munthuyo kunja ku kasupe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Apo Labani, mlongo wa Rebekayo, adaonadi chipini chija pamodzi ndi zigwinjiri pa mikono ya mlongo wakeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Tsono Rebeka anali ndi mlongo wake dzina lake Labani. Onani mutuwo |