Genesis 24:28 - Buku Lopatulika28 Namwaliyo ndipo anathamanga nawauza zimenezo kunyumba ya amake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Namwaliyo ndipo anathamanga nawauza zimenezo kunyumba ya amake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Tsono namwali uja adathamangira kunyumba kwa mai wake, nafotokozera onse nkhani yonseyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Mtsikana uja anathamanga nakafotokozera zimenezi anthu a kwa amayi ake. Onani mutuwo |