Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:28 - Buku Lopatulika

28 Namwaliyo ndipo anathamanga nawauza zimenezo kunyumba ya amake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Namwaliyo ndipo anathamanga nawauza zimenezo kunyumba ya amake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Tsono namwali uja adathamangira kunyumba kwa mai wake, nafotokozera onse nkhani yonseyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Mtsikana uja anathamanga nakafotokozera zimenezi anthu a kwa amayi ake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:28
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Rebeka anali ndi mlongo wake dzina lake Labani; ndipo Labani anathamangira munthuyo kunja ku kasupe.


Ndipo ndinawerama mutu wanga ndi kulambira Yehova, ndi kumyamikira Yehova, Mulungu wa mbuyanga Abrahamu, amene ananditsogolera ine m'njira yakuona, kuti ndikamtengere mwana wamwamuna wake mwana wa mkazi wa mphwake wa mbuyanga.


Ndipo mlongo wake ndi amake anati, Namwali akhale ndi ife masiku akuwerengeka, afikire khumi; patsogolo pake iye adzamuka.


Ndipo Isaki anamlowetsa mkaziyo m'hema wa amake Sara, namtenga Rebeka, nakhala iye mkazi wake; ndipo anamkonda iye; ndipo Isaki anatonthozedwa mtima atafa amake.


Ndipo Yakobo anamuuza Rakele kuti iye ndiye mbale wake wa atate wake, kuti ndiye mwana wake wa Rebeka, ndipo Rakele anathamanga nakauza atate wake.


Ndipo Labani analowa m'hema wa Yakobo, ndi m'hema wa Leya, ndi m'mahema a adzakazi awiri aja; koma sanapeze. Ndipo anatuluka m'hema wa Leya nalowa m'hema wa Rakele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa