Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:25 - Buku Lopatulika

25 Natinso kwa iye, Tili nao udzu ndi zakudya zambiri ndi malo ogona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Natinso kwa iye, Tili nao udzu ndi zakudya zambiri ndi malo ogona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 “Chakudya chodyetsa nyamazi chiliko kwathu, ndipo malo oti inu mugoneko aliponso.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ndipo anapitiriza kunena kuti, “Chakudya chodyetsa nyamazi chilipo kwathu ndipo malo woti mugone aliponso.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:25
8 Mawu Ofanana  

Ndipo mkaziyo anati kwa iye, Ine ndine mwana wa Betuele mwana wamwamuna wa Milika, amene anambalira Nahori.


Munthuyo ndipo anawerama mutu namyamika Yehova.


Munthuyo ndipo analowa m'nyumba, namasula ngamira, napatsa ngamira udzu ndi chakudya, ndi madzi akusamba mapazi ake ndi mapazi a iwo amene anali naye.


Ndipo pamene wina wa iwo anamasula thumba lake kuti adyetse bulu wake pachigono, anapeza ndalama zake; taonani, zinali kukamwa kwa thumba lake.


Koma mfulu aganizira zaufulu, nakhazikika m'zaufulu zomwe.


mucherezane wina ndi mnzake, osadandaula:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa