Genesis 24:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo mkaziyo anati kwa iye, Ine ndine mwana wa Betuele mwana wamwamuna wa Milika, amene anambalira Nahori. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo mkaziyo anati kwa iye, Ine ndine mwana wa Betuele mwana wamwamuna wa Milika, amene anambalira Nahori. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 “Ine ndine mwana wa Betuele, mwana wa Nahori, amene adamubalira Milika.” Adapitiriranso kunena kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Anamuyankha kuti, “Ine ndine mwana wa Betueli, mwana amene Milika anaberekera Nahori.” Onani mutuwo |