Genesis 22:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Abrahamu anati kwa anyamata ake, Khalani kuno ndi bulu, ine ndi mwanayu tinka uko, ndipo tikapemphera ndi kubweranso kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Abrahamu anati kwa anyamata ake, Khalani kuno ndi bulu, ine ndi mwanayu tinka uko, ndipo tikapemphera ndi kubweranso kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndipo adauza antchito ake aja kuti, “Inu bakhalani pano ndi buluyu. Ine ndi mnyamatayu tipita uko kukapemphera, pambuyo pake tidzakupezani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo Abrahamu anati kwa antchito ake aja, “Bakhalani pano ndi buluyu. Ine ndi mnyamatayu tipita uko kukapemphera, koma tibweranso.” Onani mutuwo |