Genesis 22:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo mthenga wa Yehova anamuitana Abrahamu ndi mau odzera kumwamba kachiwiri, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo mthenga wa Yehova anamuitana Abrahamu ndi mau odzera kumwamba kachiwiri, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mngelo wa Chauta uja adamuitana Abrahamu kachiŵiri kuchokera kumwamba, adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mngelo wa Yehova anayitana Abrahamu kuchokera kumwamba kachiwiri Onani mutuwo |