Genesis 22:16 - Buku Lopatulika16 nati, Pa Ine ndekha ndalumbira, ati Yehova, popeza wachita ichi, sunandikanize mwana wako, mwana wako yekha, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 nati, Pa Ine ndekha ndalumbira, ati Yehova, popeza wachita ichi, sunandikaniza mwana wako, mwana wako yekha, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 “Chauta akunena kuti, ‘Ndikulumbira kuti ndidzakudalitsa kwambiri iwe chifukwa wachita zimenezi, osandimana mwana wako mmodzi yekha uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 ndipo anati, “Ndikulumbira mwa Ine ndekha kuti popeza wachita zimenezi, wosandikaniza mwana wako mmodzi yekhayu, Onani mutuwo |