Genesis 21:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Abimeleki anati kwa Abrahamu, Nanga anaankhosa aakazi asanu ndi awiri amene wapatula pa okha? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Abimeleki anati kwa Abrahamu, Nanga anaankhosa akazi asanu ndi awiri amene wapatula pa okha? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Abimeleki adamufunsa kuti “Chifukwa chiyani mukuchita zimenezi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 ndipo Abimeleki anafunsa Abrahamu, “Kodi tanthauzo lake la ana ankhosa aakazi asanu ndi awiri amene wawapatula pawokhawa nʼchiyani?” Onani mutuwo |