Genesis 21:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo mwana wamwamuna wa mdzakazi uyo ndidzayesa mtundu, chifukwa iye ndiye mbeu yako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo mwana wamwamuna wa mdzakazi uyo ndidzayesa mtundu, chifukwa iye ndiye mbeu yako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mwana wa mdzakaziyunso ndidzampatsa ana ambiri, ndipo adzasanduka mtundu ndithu, popeza kuti iyeyunso ndi mwana wako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mwana wa mdzakazi wakoyu ndidzamusandutsa mtundu wa anthu chifukwa ndi mwana wako.” Onani mutuwo |