Genesis 20:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Abrahamu anati za Sara mkazi wake, Iye ndiye mlongo wanga: ndipo Abimeleki mfumu ya Gerari anatumiza namtenga Sara Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Abrahamu anati za Sara mkazi wake, Iye ndiye mlongo wanga: ndipo Abimeleki mfumu ya Gerari anatumiza namtenga Sara Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kumeneko adauza anthu kuti, “Sarayu ndi mlongo wanga.” Motero Abimeleki, mfumu ya ku Gerari, adamtenga Sarayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndipo Abrahamu ankawawuza za Sara kuti, “Iyeyu ndi mlongo wanga.” Choncho Abimeleki, mfumu wa ku Gerari anamutenga Sara uja. Onani mutuwo |