Genesis 20:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti Yehova anatseketsa mimba yonse ya a m'nyumba ya Abimeleki, chifukwa cha Sara mkazi wake wa Abrahamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti Yehova anatseketsa mimba yonse ya a m'nyumba ya Abimeleki, chifukwa cha Sara mkazi wake wa Abrahamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndiye kuti Chauta anali ataŵatseka akazi onse a m'banja la Abimeleki kuti akhale osabala, chifukwa cha Sara mdzakazi wa Abrahamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Paja Yehova nʼkuti atatseka akazi onse a mʼbanja la Abimeleki kuti asabereke ana chifukwa cha Sara, mkazi wa Abrahamu. Onani mutuwo |