Genesis 2:17 - Buku Lopatulika17 koma mtengo wakudziwitsa zabwino ndi zoipa usadye umenewo; chifukwa tsiku lomwe udzadya umenewo udzafa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 koma mtengo wakudziwitsa zabwino ndi zoipa usadye umenewo; chifukwa tsiku lomwe udzadya umenewo udzafa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 kupatula mtengo wokhawo umene umadziŵitsa zabwino ndi zoipa. Zipatso za mtengo umenewo usadye. Ukadzadya, ndithu udzafa!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 koma usadye zipatso za mu mtengo wodziwitsa chabwino ndi choyipa, popeza ukadzadya za mu mtengowu udzafa ndithu.” Onani mutuwo |