Genesis 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo zinatha kupangidwa zakumwamba ndi dziko lapansi, ndi khamu lao lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo zinatha kupangidwa zakumwamba ndi dziko lapansi, ndi khamu lao lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Motero dziko lonse lapansi, thambo ndi zonse zokhala m'menemo, zidatha kulengedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Motero kumwamba, dziko lapansi ndi zonse za mʼmenemo zinatha kulengedwa monga mwa kuchuluka kwawo. Onani mutuwo |