Genesis 19:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anati, Abale anga, musachitetu koipa kotere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anati, Abale anga, musachitetu koipa kotere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono adaŵapempha kuti, “Inu abwenzi anga, musachite zimenezi chifukwa nkulakwa kwambiri kuchita zotere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 ndipo anati, “Ayi anzanga, musachite zinthu zoyipa zotere. Onani mutuwo |