Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 19:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Loti anatulukira kwa iwo pakhomo, natseka chambuyo pakhomo pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Loti anatulukira kwa iwo pakhomo, natseka chambuyo pakhomo pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Loti adatuluka panja natseka chitseko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Loti anatuluka panja kukakumana nawo natseka chitseko

Onani mutuwo Koperani




Genesis 19:6
3 Mawu Ofanana  

ndipo anamuitana Loti, nati kwa iye, Ali kuti anthu amene anadza kwa iwe madzulo ano, utitulutsire iwo kuti tiwadziwe.


Ndipo anati, Abale anga, musachitetu koipa kotere.


Ndipo munthu mwini nyumba anawatulukira nanena nao, Iai, abale anga, musachite choipa chotere; popeza mwamuna uyu walowa m'nyumba mwanga, musachite chopusa ichi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa