Genesis 19:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo Loti anabwera kutuluka mu Zowari nakhala m'phiri ndi ana aakazi awiri pamodzi naye: chifukwa anaopa kukhala mu Zowari, ndipo anakhala m'phanga, iye ndi ana ake aakazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo Loti anabwera kutuluka m'Zowari nakhala m'phiri ndi ana akazi awiri pamodzi naye: chifukwa anaopa kukhala m'Zowari, ndipo anakhala m'phanga, iye ndi ana ake akazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Popeza kuti Loti ankaopa kukhala ku Zowari, iyeyo pamodzi ndi ana ake aakazi aŵiri aja, adapita ku dziko lamapiri, onsewo nkumakakhala m'mapanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Loti ndi ana ake awiri aakazi anachoka ku Zowari nakakhala ku mapiri, chifukwa amachita mantha kukhala ku Zowari. Iye ndi ana ake awiri ankakhala mʼphanga. Onani mutuwo |