Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 19:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa kunka kumalo kumene anaima pamaso pa Yehova:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa kunka kumalo kumene anaima pamaso pa Yehova:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 M'maŵa mwake, m'mamaŵa, Abrahamu adathamangira ku malo omwe aja, kumene adaaimirira pamaso pa Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Mmawa mwake, Abrahamu ananyamuka nabwerera kumalo kumene anakumana ndi Yehova kuja.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 19:27
6 Mawu Ofanana  

ndipo anayang'anira ku Sodomu ndi ku Gomora ndi ku dziko lonse la chigwa, ndipo anapenya, taonanitu, utsi wa dzikolo unakwera, monga utsi wa ng'anjo.


M'mawa, Yehova, mudzamva mau anga; m'mawa, ndidzakukonzerani pemphero langa, ndipo ndidzadikira.


Ndidzaima pa dindiro langa ndi kudziika palinga, ndipo ndidzayang'anira ndione ngati adzanenanji mwa ine, ngatinso ndidzamyankha chiyani pa choneneza changa.


Mwa ichi tiyenera kusamaliradi zimene tidazimvazi kuti kapena tingatengedwe ndi kusiyana nazo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa