Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 19:26 - Buku Lopatulika

26 Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Koma mkazi wa Loti adaacheukira m'mbuyo, ndiye pomwepo adasanduka mwala wamchere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Koma mkazi wa Loti anachewuka ndipo anasanduka mwala wa mchere.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 19:26
5 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.


Wobwerera m'mbuyo m'mtima adzakhuta njira yake; koma munthu wabwino adzakhuta za mwa iye yekha.


mbale zofukizazo za iwo amene adachimwira moyo waowao, ndipo azisule zaphanthiphanthi, zikhale chivundikiro cha guwa la nsembe; popeza anabwera nazo pamaso pa Yehova, chifukwa chake zikhala zopatulika; ndipo zidzakhala chizindikiro kwa ana a Israele.


Koma wolungama wangayo adzakhala ndi moyo wochokera m'chikhulupiriro: Ndipo ngati abwerera, moyo wanga ulibe kukondwera mwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa