Genesis 19:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Yehova anavumbitsa pa Sodomu ndi pa Gomora miyala ya sulufure ndi moto kutuluka kwa Mulungu kumwamba; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Yehova anavumbitsa pa Sodomu ndi pa Gomora miyala ya sulufure ndi moto kutuluka kwa Mulungu kumwamba; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tsono Chauta adagwetsa moto wa sulufule pa Sodomu ndi Gomora kuchokera kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ndiye Yehova anathira sulufule wamoto wochokera kumwamba kwa Yehova pa Sodomu ndi Gomora. Onani mutuwo |
Chifukwa chake, pali moyo wanga, ati Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele, Zedi Mowabu adzakhala ngati Sodomu, ndi ana a Amoni ngati Gomora, pochuluka khwisa ndi maenje a mchere, ndi bwinja losatha; otsala a anthu anga adzalanda zao, ndi otsala a mtundu wa anthu anga adzawalandira akhale cholowa chao.