Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 19:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo dzuwa lidakwera padziko pamene Loti anafika ku Zowari.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo dzuwa lidakwera pa dziko pamene Loti anafika ku Zowari.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Pamene dzuŵa linkatuluka, Loti nkuti atafika kale ku Zowari.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Pamene Loti amafika ku Zowari, nʼkuti dzuwa litatuluka.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 19:23
3 Mawu Ofanana  

Fulumira, thawira kumeneko; pakuti sindithai kuchita kanthu usadafike kumeneko. Chifukwa chake anatcha dzina la mzindawo Zowari.


Ndipo Yehova anavumbitsa pa Sodomu ndi pa Gomora miyala ya sulufure ndi moto kutuluka kwa Mulungu kumwamba;


Ndipo kudamchera iye pamene anaoloka pa Penuwele, ndipo iye anatsimphina ndi ntchafu yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa