Genesis 18:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Abrahamu analowa msanga m'hema wake kwa Sara, nati, Konza msanga miyeso itatu ya ufa wosalala, nuumbe, nupange mikate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Abrahamu analowa msanga m'hema wake kwa Sara, nati, Konza msanga miyeso itatu ya ufa wosalala, nuumbe, nupange mikate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Abrahamu adaloŵa msangamsanga m'hema, nauza Sara kuti “Utenge msanga nsengwa zitatu za ufa wosalala, uukande ndi kupanga buledi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Choncho Abrahamu anafulumira kupita kwa Sara mʼtenti nati, “Tafulumira, tenga mabeseni atatu a ufa wosalala, ukande ndi kupanga buledi.” Onani mutuwo |