Genesis 18:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Apo Abrahamu adayandikira kwa Chauta namufunsa kuti, “Kodi monga mudzaonongadi anthu osachimwa pamodzi ndi ochimwa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Kenaka Abrahamu anasendera kufupi ndi Iye nati, “Kodi mudzawonongera kumodzi wolungama ndi woyipa? Onani mutuwo |