Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 17:26 - Buku Lopatulika

26 Tsiku lomwelo anadulidwa Abrahamu ndi Ismaele mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Tsiku lomwelo anadulidwa Abrahamu ndi Ismaele mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Pa tsiku limeneli Abrahamu ndi mwana wake Ismaele adaumbalidwa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Onse, Abrahamu ndi mwana wake Ismaeli, anachita mdulidwe tsiku limodzi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 17:26
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuka Abramu monga Yehova ananena kwa iye, ndipo Loti anamuka pamodzi naye: ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi awiri kudza zisanu, pamene anatuluka mu Harani.


Ndipo Ismaele mwana wake anali wa zaka khumi ndi zitatu pamene anadulidwa m'khungu lake.


Ndipo amuna onse a m'nyumba mwake obadwa m'nyumba, ndi ogulidwa ndi ndalama kwa alendo, anadulidwa pamodzi naye.


Ndinafulumira, osachedwa, kusamalira malamulo anu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa