Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 17:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo Ismaele mwana wake anali wa zaka khumi ndi zitatu pamene anadulidwa m'khungu lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo Ismaele mwana wake anali wa zaka khumi ndi zitatu pamene anadulidwa m'khungu lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Mwana wake Ismaele anali wa zaka 13 pamene adaumbalidwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 ndipo mwana wake Ismaeli anali ndi zaka khumi ndi zitatu;

Onani mutuwo Koperani




Genesis 17:25
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Hagara anambalira Abramu mwana wamwamuna ndipo Abramu anatcha dzina la mwana wake amene anambalira iye Hagara, Ismaele.


Ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi, pamene Hagara anambalira Abramu Ismaele.


Tsiku lomwelo anadulidwa Abrahamu ndi Ismaele mwana wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa