Genesis 17:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Abrahamu anali wa zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zinai, pamene anadulidwa m'khungu lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Abrahamu anali wa zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zinai, pamene anadulidwa m'khungu lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Abrahamu anali wa zaka 99 pa nthaŵi imene adaumbalidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Abrahamu anali ndi zaka 99 pamene anachita mdulidwe, Onani mutuwo |