Genesis 16:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Bwera kwa wakuka wako, udzichepetse wekha pamanja pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Bwera kwa wakuka wako, udzichepetse wekha pamanja pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mngelo wa Chautayo adati, “Iyai, bwerera kwa Sarai, ukamgonjere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mngelo wa Yehova anamuwuza kuti, “Bwerera kwa mbuye wako ndipo ukamugonjere. Onani mutuwo |