Genesis 16:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Hagara anambalira Abramu mwana wamwamuna ndipo Abramu anatcha dzina la mwana wake amene anambalira iye Hagara, Ismaele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Hagara anambalira Abramu mwana wamwamuna ndipo Abramu anatcha dzina la mwana wake amene anambalira iye Hagara, Ismaele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono Hagara adamubalira Abramu mwana wamwamuna, namutcha dzina loti Ismaele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Tsono Hagara anamuberekera Abramu mwana wamwamuna ndipo Abramu anamutcha mwanayo Ismaeli. Onani mutuwo |