Genesis 16:14 - Buku Lopatulika14 Chifukwa chake chitsimecho chinatchedwa Beere-Lahai-Roi; taonani chili pakati pa Kadesi ndi Beredi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Chifukwa chake chitsimecho chinatchedwa Beere-Lahai-Roi; taonani chili pakati pa Kadesi ndi Beredi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Nchifukwa chake anthu amachitchula chitsime cha pakati pa Kadesi ndi Beredi kuti Chitsime cha Wamoyo-Wondipenya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Nʼchifukwa chake chitsime chija chimene chili pakati pa Kadesi ndi Beredi chinatchedwa Beeri-lahai-roi. Onani mutuwo |