Genesis 16:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi, pamene Hagara anambalira Abramu Ismaele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi, pamene Hagara anambalira Abramu Ismaele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Abramu anali wa zake 86 pa nthaŵi imeneyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pamene Hagara anamubalira Ismaeli nʼkuti Abramuyo ali ndi zaka 86. Onani mutuwo |