Genesis 13:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Abramu anasuntha hema wake nafika nakhala pa mitengo yathundu ya pa Mamure, imene ili mu Hebroni, nammangira Yehova kumeneko guwa la nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Abramu anasuntha hema wake nafika nakhala pa mitengo yathundu ya pa Mamure, imene ili m'Hebroni, nammangira Yehova kumeneko guwa la nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Motero Abramu adazula hema lake, nakakhala patsinde pa mitengo ya thundu ya ku Mamure, imene ili ku Hebroni. Ndipo kumeneko adamangira Chauta guwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Choncho Abramu anasamutsa tenti yake napita kukakhala pafupi ndi mitengo ikuluikulu ija ya thundu ya ku Mamre ku Hebroni, kumene anamangira Yehova guwa lansembe. Onani mutuwo |