Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:21 - Buku Lopatulika

21 ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi ziwiri, atabala Serugi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi ziwiri, atabala Serugi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Pambuyo pake adakhala ndi moyo zaka zina 207, ndipo adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Atabereka Serugi, Reu anakhala ndi moyo zaka zina 207 ndipo anali ndi ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:21
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza ziwiri, nabala Serugi:


Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa