Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:22 - Buku Lopatulika

22 Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Serugi ali wa zaka 30, adabereka mwana dzina lake Nahori.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Pamene Serugi anali ndi zaka makumi atatu, anabereka Nahori.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:22
3 Mawu Ofanana  

ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi ziwiri, atabala Serugi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka mazana awiri, atabala Nahori, nabala ana aamuna ndi aakazi.


Ndipo Yoswa ananena ndi anthu onse, Atero Yehova Mulungu wa Israele, Kale lija makolo anu anakhala tsidya lija la mtsinje, ndiye Tera, atate wa Abrahamu ndi atate wa Nahori; natumikira milungu ina iwowa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa