Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 10:3 - Buku Lopatulika

3 Ndi ana aamuna a Gomeri: Asikenazi, ndi Rifati, ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndi ana amuna a Gomeri: Asikenazi, ndi Rifati, ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Ana a Gomeri anali Asikenazi, Rifati ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 10:3
4 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Gomeri: Asikenazi, Difati, ndi Togarima.


Kwezani mbendera m'dziko, ombani lipenga mwa amitundu, konzerani amitundu amenyane naye, mummemezere maufumu a Ararati, Mini, ndi Asikenazi; muike nduna; amenyane naye; mukweretse akavalo ngati dzombe.


Iwo a nyumba ya Togarima anagula malonda ako ndi akavalo, ndi akavalo a nkhondo, ndi nyuru.


Gomeri ndi magulu ake onse, nyumba ya Togarima, ku malekezero a kumpoto, ndi magulu ake onse, mitundu yambiri pamodzi ndi iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa