Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 10:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Ndi ana aamuna a Gomeri: Asikenazi, ndi Rifati, ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndi ana amuna a Gomeri: Asikenazi, ndi Rifati, ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Ana a Gomeri anali Asikenazi, Rifati ndi Togarima.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 10:3
4 Mawu Ofanana  

Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima


“Kwezani mbendera ya nkhondo mʼdziko! Lizani lipenga pakati pa mitundu ya anthu! Konzekeretsani mitundu ya anthu kuti ikamuthire nkhondo; itanani maufumu awa: Ararati, Mini ndi Asikenazi kuti adzamuthire nkhondo. Ikani mtsogoleri wankhondo kuti amenyane naye; tumizani akavalo ochuluka ngati magulu a dzombe.


“Anthu a ku Beti Togarima ankapereka akavalo antchito, akavalo ankhondo ndi abulu mosinthanitsa ndi katundu wako.


Padzakhalanso Gomeri pamodzi ndi ankhondo ake onse ndiponso banja la Togarima ndi gulu lake lonse lankhondo lochokera kutali kumpoto. Padzakhaladi mitundu yambiri ya anthu pamodzi ndi iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa