Filemoni 1:22 - Buku Lopatulika22 Koma undikonzerenso pogona; pakuti ndiyembekeza kuti mwa mapemphero anu ndidzapatsidwa kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma undikonzerenso pogona; pakuti ndiyembekeza kuti mwa mapemphero anu ndidzapatsidwa kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Kanthu kenanso ndi aka: undikonzere malo, chifukwa ndikhulupirira kuti Mulungu adzamvera mapemphero a inu nonse, ndi kundibwezera kwa inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Chinthu chinanso ndi ichi: undikonzere malo, chifukwa ndikukhulupirira kuti Mulungu adzamvera mapemphero anu ndi kundibwezera kwa inu. Onani mutuwo |