Filemoni 1:20 - Buku Lopatulika20 Inde, mbale, ndikondwere nawe mwa Ambuye: utsitsimutse mtima wanga mwa Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Inde, mbale, ndikondwere nawe mwa Ambuye: utsitsimutse mtima wanga mwa Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tsono, mbale wanga, inenso undithandizeko chifukwa cha Ambuye. Undisangulutseko ngati mbale mwa Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mʼbale, ndikufuna kuti ndipindule nawe mwa Ambuye; tsono tsitsimutsa mtima wanga mwa Khristu. Onani mutuwo |