Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Filemoni 1:15 - Buku Lopatulika

15 Pakuti kapena anasiyanitsidwa ndi iwe kanthawi chifukwa cha ichi, ndi kuti udzakhala naye nthawi zonse;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Pakuti kapena anasiyanitsidwa ndi iwe kanthawi chifukwa cha ichi, ndi kuti udzakhala naye nthawi zonse;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Kapena Onesimo adangokusiya kanthaŵi pang'ono, kuti udzakhale naye nthaŵi zonse,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani




Filemoni 1:15
5 Mawu Ofanana  

Koma inu, munandipangira ine choipa; koma Mulungu anachipangira chabwino, kuti kuchitike monga lero, kupulumutsa amoyo anthu ambiri.


Indedi, kuzaza kwake kwa munthu kudzakulemekezani; chotsalira cha kuzazaku mudzachiletsa.


Ndipo wokhala m'mphepete mwa nyanja muno adzati tsiku limenelo, Taonani, kuyembekeza kwathu kuli kotero, kumene ife tinathawira atithangate kupulumutsidwa kwa mfumu ya Asiriya, ndipo ife tidzapulumuka bwanji?


kuti achite zilizonse dzanja lanu ndi uphungu wanu zidaweruziratu zichitike.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa