Eksodo 9:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Yehova anaika nthawi yakuti, nati, Mawa Yehova adzachita chinthu ichi m'dzikomu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Yehova anaika nthawi yakuti, nati, Mawa Yehova adzachita chinthu ichi m'dzikomu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chauta waika nthaŵi, ndipo akunena kuti zimenezi azichita maŵa.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova anayika nthawi ndipo anati, “Yehova adzachita zimenezi mmawa mʼdziko muno.” Onani mutuwo |