Eksodo 8:32 - Buku Lopatulika32 Koma Farao anaumitsa mtima wake nthawi yomweyonso, ndipo sanalole anthu amuke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Koma Farao anaumitsa mtima wake nthawi yomweyonso, ndipo sanalola anthu amuke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Koma ngakhale pa nthaŵi imeneyinso, Farao adakhala wokanikabe, ndipo sadalole kuti Aisraele apite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Koma nthawi imeneyinso Farao anawumitsa mtima wake ndipo sanalole kuti anthu atuluke. Onani mutuwo |