Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 7:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsono Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 7:8
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu, ndi Aroni anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu kudza zitatu, pamene ananena ndi Farao.


Pamene Farao adzalankhula nanu, ndi kuti, Dzichitireni chodabwitsa; pamenepo uzinena ndi Aroni, Tenga ndodo yako, iponye pansi pamaso pa Farao, isanduke chinjoka.


ndi zizindikiro zake, ndi ntchito zake, adazichitira Farao mfumu ya Aejipito, ndi dziko lake lonse pakati pa Ejipito;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa