Eksodo 7:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Mose anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu, ndi Aroni anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu kudza zitatu, pamene ananena ndi Farao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Mose anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu, ndi Aroni anali nazo zaka makumi asanu ndi atatu kudza zitatu, pamene ananena ndi Farao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pamenepo nkuti Mose ali wa zaka 80 ndipo Aroni wa zaka 83, pa nthaŵi imene ankalankhula ndi Farao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mose anali ndi zaka 80, ndipo Aaroni anali ndi zaka 83 pamene anakayankhula kwa Farao. Onani mutuwo |