Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 6:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo ana aamuna a Merari ndiwo: Mali ndi Musi. Amenewo ndiwo mabanja a Levi mwa kubadwa kwao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo ana amuna a Merari ndiwo: Mali ndi Musi. Amenewo ndiwo mabanja a Levi mwa kubadwa kwao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Ana a Merari naŵa: Mali ndi Musi. Ameneŵa ndiwo mabanja a Levi pamodzi ndi zidzukulu zao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Ana a Merari anali Mali ndi Musi. Awa anali mafuko a Levi monga mwa mibado yawo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 6:19
7 Mawu Ofanana  

Ana a Merari: Mali ndi Musi. Ndi ana a Mali: Eleazara ndi Kisi.


Ana a Musi: Mali, ndi Edere, ndi Yeremoti; atatu.


Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.


Ana a Merari: Mali ndi Musi. Ndi mabanja a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao ndi awa.


Ndipo ana a Levi maina ao ndi awa: Geresoni, ndi Kohati ndi Merari.


Ndi ana a Merari monga mwa mabanja ao: Mali ndi Musi. Awa ndi mabanja a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao.


Ana a Merari, monga mwa mabanja ao, analandira motapa pa fuko la Rubeni, ndi pa fuko la Gadi, ndi pa fuko la Zebuloni mizinda khumi ndi iwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa